Levitiko 25:51-54 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

51. Zikamtsalira zaka zambiri, monga mwa izi abwezere ndarama zakumuombola zocokera ku ndalama zomgulazo.

52. Ndipo zikamtsalira zaka pang'ono kufikira caka coliza lipenga amwerengere; monga mwa zaka zace abwezere mtengo wace wakumuombola.

53. Akhale naye monga wolipidwa caka ndi caka; asamamlamulira momzunza pamaso pako,

54. Ndipo akapanda kumuombola motero, azituruka caka coliza lipenga, iye ndi ana ace omwe.

Levitiko 25