Levitiko 25:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Yehova ananena ndi Mose m'phiri la Sinai, ndi kuti,

2. Nena ndi ana a Israyeli, nuti nao, Mutakalowa m'dziko limene ndikupatsani, dzikoli lizisungira Yehova Sabata.

3. Zaka zisanu ndi cimodzi ubzale m'munda mwako, ndi zaka zisanu ndi cimodzi udzombole mphesa zako, ndi kuceka zipatso zace;

Levitiko 25