Levitiko 23:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi wansembe awaweyule, pamodzi ndi mkate wa zipatso zoyamba, nsembe yoweyula pamaso pa Yehova, pamodzi ndi ana a nkhosa awiriwo; zikhale zopatulikira Yehova, kuti zikhale za wansembe.

Levitiko 23

Levitiko 23:17-28