Levitiko 21:23-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. koma asafike ku nsaru yocinga, asayandikize ku guwa la nsembe, popeza ali naco cirema; kuti angaipse malo anga opatulika; popeza Ine ndine Yehova wakuwapatula.

24. Momwemo Mose ananena ndi Aroni, ndi ana ace amuna, ndi ana onse a Israyeli.

Levitiko 21