Levitiko 21:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma asafike ku nsaru yocinga, asayandikize ku guwa la nsembe, popeza ali naco cirema; kuti angaipse malo anga opatulika; popeza Ine ndine Yehova wakuwapatula.

Levitiko 21

Levitiko 21:18-24