Hoseya 14:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Efraimu adzati, Ndiri ndi cianinso ndi mafano? Ndayankha, ndidzampenyerera; ndiri ngati mtengo wamlombwa wabiriwiri; zipatso zako zipezeka zocokera kwa Ine.

Hoseya 14

Hoseya 14:1-9