Genesis 22:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anafika kumalo komwe Mulungu anamuuza iye; ndipo Abrahamu anamanga guwa la nsembe nakonza nkhuni, namanga Isake mwana wace, namuika iye pa guwa la nsembe pamwamba pa nkhuni.

Genesis 22

Genesis 22:6-18