Genesis 2:11-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Dzina la wakuyamba ndi Pisoni: umenewo ndiwo wozungulira dziko lonse la Havila, m'mene muli golidi;

12. golidi wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.

13. Dzina la mtsinje waciwiri ndi Gihoni: umenewo ndiwo wozungulira dziko lonse la Kusi.

Genesis 2