Ezekieli 7:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Katsala kamphindi, ndipo ndidzakutsanulira ukali wanga, ndi kukukwaniritsira mkwiyo wanga, ndi kukuweruza monga mwa njira zako, ndipo ndidzakubwezera zonyansa zako zonse.

Ezekieli 7

Ezekieli 7:6-9