Ezekieli 48:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi ku mbali ya kum'mawa zikwi zinai mphambu mazana asanu, ndi zipata zitatu: cipata cimodzi ca Yosefe, cipata cimodzi ca Benjamini, cipata cimodzi ca Dani;

Ezekieli 48

Ezekieli 48:23-33