Ezekieli 44:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo asayandikire kwa Ine kundigwirira nchito ya nsembe, kapena kuyandikira zopatulika zanga ziri zonse zopatulikitsazo; koma azisenza manyazi ao, ndi zonyansa zao anazicita.

Ezekieli 44

Ezekieli 44:7-21