Ezekieli 38:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo udzakwerera anthu anga Israyeli ngati mtambo wakuphimba dziko; kudzacitika masiku otsiriza ndidzabwera nawe ulimbane nalo dziko langa, kuti amitundu andidziwe, pozindikiridwa Ine woyera mwa iwe, Gogi, pamaso pao.

Ezekieli 38

Ezekieli 38:15-23