Ezekieli 35:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

cifukwa cace, Pali Ine, ati Ambuye Yehova, ndidzacita monga mwa mkwiyo wako, ndi monga mwa nsanje yako unacita nayo pa kukwiya nao iwe; ndipo ndidzadziwika nao pamene ndikuweruza.

Ezekieli 35

Ezekieli 35:8-15