Ezekieli 30:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace atero Ambuye Yehova, Taona, Ine ndilimbana naye Parao mfumu ya Aigupto, ndidzatyola manja ace, lolimba ndi lotyokalo, ndi kutayitsa lupanga m'dzanja lace.

Ezekieli 30

Ezekieli 30:13-26