Ezekieli 27:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Damasiko anagulana nawe malonda cifukwa ca zambirizo udazipanga, cifukwa ca kucuruka kwa cuma ciri conse, ndi vinyo wa ku Keliboni, ndi ubweya wa nkhosa woyera.

Ezekieli 27

Ezekieli 27:15-21