Ezekieli 22:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wina anacita conyansa ndi mkazi wa mnansi wace, winanso wadetsa mpongozi wace mwamanyazi, ndi wina mwa iwe anaipitsa mlongo wace mwana wamkazi wa atate wace.

Ezekieli 22

Ezekieli 22:8-17