Ezekieli 19:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo unali nazo ndodo zolimba zikhale ndodo zacifumu, za ocita ufumu, ndi msinkhu wao unakula kufikira kumitambo, nizinaoneka m'kusomphoka kwao pakati pa nthambi zace zambiri.

Ezekieli 19

Ezekieli 19:2-14