Ezekieli 18:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma inu mukuti, Alekeranji mwana kusenza mphulupulu za atate wace? Mwanayo akacita ciweruzo ndi cilungamo, nakasunga malemba anga onse, ndi kuwacita, adzakhala ndi moyo ndithu.

Ezekieli 18

Ezekieli 18:12-29