Ezekieli 17:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Uziti, Atero Ambuye Yehova, Udzakondwa kodi? sadzausula ndi kudula zipatso zace, kuti uume, kuti masamba ace onse ophuka aume, ngakhale palibe mphamvu yaikuru, kapena anthu ambiri akuuzula?

Ezekieli 17

Ezekieli 17:3-19