Ezekieli 16:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi mbiri yako inabuka mwa amitundu cifukwa ca kukongola kwako; pakuti ndiko kwangwiro, mwa ulemerero wanga ndinauika pa iwe, ati Ambuye Yehova.

Ezekieli 16

Ezekieli 16:11-20