Ezara 2:68 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo akulu ena a nyumba za makolo, pofika ku nyumba ya Yehova iri ku Yerusalemu, anapereka caufulu kwa nyumba ya Mulungu cakulimika pakuzika pace.

Ezara 2

Ezara 2:62-70