Ezara 1:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo ananyamuka akulu a nyumba za makolo a Yuda ndi Benjamini, ndi ansembe, ndi Alevi, ndiwo onse amene Mulungu adawautsira mzimu wao akwere kukamanga nyumba ya Yehova iri ku Yerusalemu.

Ezara 1

Ezara 1:1-6