Estere 7:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nayankha mkazi wamkuru Estere, nati, Ngati mwandikomera mtima, mfumu, ndipo cikakomera mfumu, andilekere moyo wanga pa kupempha kwanga, ndi wa anthu a mtundu wanga pa pempho langa;

Estere 7

Estere 7:1-9