Eksodo 6:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Yehova ananena kwa Mose, Tsopano udzaona comwe ndidzacitira Farao; pakuti ndi dzanja lamphamvu adzawalola apite, inde ndi dzanja lamphamvu adzawaingitsa m'dziko lace.

2. Ndipo Mulungu ananena ndi Mose, nati kwa iye, Ine ndine YEHOV A:

3. ndipo ndinaonekera Abrahamu, Isake ndi Yakobo, Mulungu Wamphamvuyonse; koma sindinadziwika kwa iwo ndi dzina langa YEHOV A.

Eksodo 6