Eksodo 39:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapanga mphete ziwiri zagolidi, naziika pa zapamapewa ziwiri za efodi pansi pace, pa mbali yace ya kutsogolo, pafupi pa msoko wace, pamwamba pa mpango wa efodi.

Eksodo 39

Eksodo 39:14-30