Eksodo 23:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Uzicita nchito yako masiku asanu ndi limodzi, koma tsiku lacisanu ndi ciwiri uzipumula; kuti ng'ombe yako ndi buru wako zipumule, ndi kuti mwana wa mdzakaziwako ndi mlendo atsitsimuke.

Eksodo 23

Eksodo 23:6-17