Eksodo 23:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma caka cacisanu ndi ciwiri uuleke, ugone; kuti aumphawi a anthu a mtundu wako adyemo ndipo zotsalira iwowa zoweta za kubusa zizidye; momwemo uzicita ndi munda wako wamphesa, ndimundawakowaazitona.

Eksodo 23

Eksodo 23:4-17