Eksodo 12:44-47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

44. koma kapolo wa mwini ali yense, wogula ndi ndarama, utamdula, ndipo adyeko.

45. Mlendo kapena wolembedwa nchito asadyeko.

46. Audye m'nyumba imodzi; usaturukira nayo kubwalo nyama yina; ndipo musathyole pfupa lace.

47. Msonkhano wonse wa Israyeli uzicita ici.

Eksodo 12