Eksodo 12:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

mudzati, Ndiko nsembe ya Paskha wa Yehova, amene anapitirira nyumba za ana a Israyeli m'Aigupto, pamene anakantha Aaigupto, napulumutsa nyumba zathu.

Eksodo 12

Eksodo 12:18-37