Deuteronomo 9:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Musamanena mumtima mwanu, atawapitikitsa pamaso panu Yehova Mulungu wanu, ndi kuti, Cifukwa ca cilungamo canga Yehova anandilowetsa kudzalandira dziko ili; pakuti Yehova awapitikitsa pamaso panu cifukwa ca zoipa za amitundu awa.

Deuteronomo 9

Deuteronomo 9:1-12