Deuteronomo 28:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Adzapereka ana anu amuna ndi akazi kwa anthu a mtundu wina, ndipo m'maso mwanu mudzada ndi kupenyerera, powalirira tsiku lonse; koma mulibe mphamvu m'dzanja lanu.

Deuteronomo 28

Deuteronomo 28:30-33