Deuteronomo 19:16-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Mboni yaciwawa ikaukira munthu kumneneza ndi kuti analakwa;

17. pamenepo anthu onse awiri, pakati pao pali makaniwo, aziima pamaso pa Yehova, pamaso pa ansembe ndi oweruza okhala m'masiku awa;

18. ndipo oweruza afunsitse bwino; ndipo taonani, mboniyo ikakhala mboni yonama, yomnamizira mbale wace;

Deuteronomo 19