Deuteronomo 11:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace muzisunga mau anga awa mumtima mwanu ndi m'moyo mwanu; ndi kuwamanga ngati cizindikilo pamanja panu; ndipo zikhale zapamphumi pakati pa maso anu.

Deuteronomo 11

Deuteronomo 11:13-24