Danieli 8:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mwa kucenjera kwace adzapindulitsa cinyengo m'dzanja mwace, nadzadzikuza m'mtima mwace; ndipo posatekeseka anthu, adzaononga ambiri; adzaukiranso kalonga wa akalonga, koma adzatyoledwa popanda dzanja.

Danieli 8

Danieli 8:23-27