Danieli 6:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu inakondwera kwambiri, niwauza aturutse Danieli m'dzenje. Momwemo anamturutsa Danieli m'dzenje, ndi pathupi pace sipadaoneka bala, popeza anakhulupirira Mulungu wace.

Danieli 6

Danieli 6:16-28