Danieli 12:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ambiri adzadzitsuka ndi kudziyeretsa, nadzayesedwa ndi moto; koma oipa adzacita moipa; ndipo palibe mmodzi wa oipa adzazindikira; koma aphunzitsi ndiwo adzazindikira.

Danieli 12

Danieli 12:4-13