Aroma 2:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

popeza iwo aonetsa nchito ya lamulolo yolembedwa m'mitima yao, ndipo cikumbu mtima cao cicitiranso umboni pamodzi nao, ndipo maganizo ao wina ndi mnzace anenezana kapena akanirana;

Aroma 2

Aroma 2:7-19