Amosi 2:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ndinaononga Ine pamaso pa Aamori, amene msinkhu wao unanga msinkhu wa mikungudza, nakhala nayo mphamvu ngati thundu; koma ndinaononga zipatso zao m'mwamba, ndi mizu yao pansi.

Amosi 2

Amosi 2:3-12