Akolose 2:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Penyani kuti pasakhale wina wakulanda inu ngati cuma, mwa kukonda nzeru kwace, ndi cinyengo copanda pace, potsata mwambo wa anthu, potsata zoyamba za dziko lapansi, osati potsata Kristu;

Akolose 2

Akolose 2:1-17