Afilipi 4:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ndinakondwera mwa Ambuye kwakukuru, kuti tsopano munatsitsimukanso kulingirira mtima za kwa ine, kumenekonso munalingirirako, koma munasowa pocitapo.

Afilipi 4

Afilipi 4:5-11