2 Samueli 9:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu inati, Kodi atsalanso wina wa nyumba ya Sauli kuti ndimuonetsere cifundo ca Mulungu? Ziba nanena ndi mfumu, Aliponso mwana wa Jonatani wopunduka mapazi ace.

2 Samueli 9

2 Samueli 9:1-7