2 Samueli 3:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu onse anadza kudzadyetsa Davide cakudya kukali msana; koma Davide analumbira nati, Mulungu andilange naonjezepo, ngati ndilawa mkate kapena kanthu kena, lisanalowe dzuwa.

2 Samueli 3

2 Samueli 3:28-39