2 Samueli 3:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

citani tsono, popeza Yehova analankhula za Davide, kuti, a Ndi dzanja la Davide mnyamata wanga ndidzapulumutsa anthu anga Aisrayeli ku dzanja la Afilisti, ndi ku dzanja la adani ao onse.

2 Samueli 3

2 Samueli 3:9-24