2 Samueli 23:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iye adzakhala ngati kuunika kwa m'mawa, poturuka dzuwa,M'mawa mopanda mitambo;Pamene msipu uphuka kuturuka pansi,Cifukwa ca kuwala koyera, italeka mvula.

2 Samueli 23

2 Samueli 23:1-13