2 Samueli 20:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anati kwa Abisai, Tsopano Seba mwana wa Bikri adzaticitira coipa coposa cija ca Abisalomu; utenge anyamata a mbuye wako numtsatire, kuti angapeze midzi ya malinga ndi kupulumuka osaonekanso.

2 Samueli 20

2 Samueli 20:1-9