2 Samueli 20:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anayandikira kwa mkaziyo; ndi mkaziyo anati, Ndinu Yoabu kodi? iye nayankha, Ndine amene. Pamenepo ananena naye, Imvani mau a mdzakazi wanu. Iye nayankha, Ndirikumva.

2 Samueli 20

2 Samueli 20:16-24