2 Samueli 14:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo m'lsrayeli monse munalibe wina anthu anamtama kwambiri cifukwa ca kukongola kwace monga Abisalomu; kuyambira ku mapazi kufikira pakati pa mutu wace mwa iye munalibe cirema.

2 Samueli 14

2 Samueli 14:24-30