2 Samueli 13:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anatenga ciwaya natiturutsa pamaso pace; koma anakana kudya. Ndipo Amnoni anati, Anthu onse aturuke kundisiya ine. Naturuka onse, kumsiya.

2 Samueli 13

2 Samueli 13:2-13