2 Samueli 13:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali pakutsiriza iye kulankhula, onani, pomwepo ana amuna a mfumu anafika, nakweza mau ao, nalira misozi; ndi mfumu yomwe ndi anyamata ace analira ndi kulira kwakukuru ndithu.

2 Samueli 13

2 Samueli 13:33-39