2 Samueli 13:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Amnoni anapsinjikadi nayamba kudwala cifukwa ca mlongo wace Tamara, pakuti anali namwali, ndipo Amnoni anaciyesa capatali kumcitira kanthu.

2 Samueli 13

2 Samueli 13:1-3